Numbers 4:40 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chiŵerengero chao chidakwanira 2,630 potsata mabanja ao ndiponso banja la makolo ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 2,630.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
owerengedwa ao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, ndiwo zikwi ziwiri mphambu mazana asanu ndi limodzi kudza makumi atatu.