Numbers 4:44 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chiŵerengero chao chidakwanira 3,200 potsata mabanja ao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
atawawerenga mwa mafuko ndi mabanja awo, anali 3,200.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
owerengedwa ao monga mwa mabanja ao, ndiwo zikwi zitatu ndi mazana awiri.