Philemon 1:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kale unalibe naye ntchito, koma tsopano angathe kutithandiza kwambiri tonsefe, iweyo ndi ine ndemwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene kale sanakupindulira, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anali wopanda phindu kwa iwe, koma tsopano wasanduka wa phindu kwa iwe ndi kwa inenso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene kale sanakupindulira, koma tsopano watipindulira bwino iwe ndi ine;