Philemon 1:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndikumtumizanso kwa iwe tsopano, ndipo pakutero ndikuchita ngati kukutumizira mtima wanga womwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
amene ndi yemweyo ndakubwezera iwe, ndiye mtima weniweni wa ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndikumutumizanso kwa iwe tsopano, koma potero ndikukhala ngati ndikutumiza mtima wanga weniweni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
amene ndi yemweyo ndakubwezera iwe, ndiye mtima weni weni wa ine.