Philemon 1:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimayamika Mulungu wanga nthaŵi zonse ndikamakukumbukira m'mapemphero anga.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndiyamika Mulungu wanga nthawi zonse, ndi kukumbukira iwe m'mapemphero anga,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ine ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakukumbukira iwe mʼmapemphero anga.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiyamika Mulungu wanga nthawi zonse, ndi kukumbukila iwe m'mapemphero anga,