Philippians 1:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndimayamika Mulungu wanga nthaŵi zonse ndikamakukumbukirani.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndiyamika Mulungu wanga pokumbukira inu ponse;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndimayamika Mulungu wanga nthawi zonse ndikakumbukira inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiyamika Mulungu wanga pokumbukira inu ponse;