Philippians 2:20 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndilibenso wina wonga amene ali ndi mtima wosamala za inu kwenikweni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti ndilibe wina wa mtima womwewo, amene adzasamalira za kwa inu ndi mtima woona.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndilibenso wina monga iyeyu amene ali ndi chidwi chenicheni pa za moyo wanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti ndiribe wina wa mtima womwewo, amene adza: samalira za kwa inu ndi mtima woona.