Philippians 2:26 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsonotu akukulakalakani nonsenu, ndipo ndi wokhumudwa podziŵa kuti inu mudamva zoti iye ankadwala.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
popeza anali wolakalaka inu nonse, navutika mtima chifukwa mudamva kuti anadwala.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti akukulakalakani nonsenu ndipo akusauka mu mtima chifukwa munamva kuti akudwala.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
popeza anali wolakalaka inu nonse, nabvutika mtima cifukwa mudamva kuti anadwala.