Philippians 2:9 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa cha chimenechi Mulungu adamkweza kopambana, nampatsa dzina lopambana dzina lina lililonse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwa ichinso Mulungu anamkwezetsa Iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho Mulungu anamukweza Iye kukhala wapamwamba kwambiri, ndipo anamupatsa dzina loposa dzina lina lililonse
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwa icinso Mulungu anamkwezetsa iye, nampatsa dzina limene liposa maina onse,