Philippians 4:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akukupatsani moni anthu onse a Mulungu amene ali kuno, makamakanso ogwira ntchito ku nyumba ya Mfumu ya ku Roma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Oyera mtima onse alankhula inu, koma makamaka iwo a banja la Kaisara.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Oyera mtima onse akupereka moni, makamaka iwo a ku nyumba ya Kaisara.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Oyera mtima onse alankhula inu, koma makamaka-fwo a banja la Kaisara.