Proverbs 1:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana wanga, anthu oipa akafuna kukukopa, usamaŵamvera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwananga, akakukopa ochimwa usalole.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mwana wanga, ngati anthu oyipa afuna kukukopa usamawamvere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwananga, akakukopa ocimwa usalole.