Proverbs 1:29 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Popeza kuti mudadana ndi nzeru, ndipo simudasankhe kuwopa Chauta,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
chifukwa anada nzeru, sanafune kuopa Yehova;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Popeza iwo anadana ndi chidziwitso ndipo sanasankhe kuopa Yehova,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa anada nzeru, Sanafuna kuopa Yehova;