Proverbs 10:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Miyambo ya Solomoni: Mwana wanzeru amakondweretsa atate ake, koma mwana wopusa amanyoza amai ake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Miyambo ya Solomoni: Mwana wanzeru akondweretsa atate; koma mwana wopusa amvetsa amake chisoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Miyambo ya Solomoni: Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake, koma mwana wopusa amamvetsa amayi ake chisoni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwana wanzeru akondweretsa atate; Koma mwana wopusa amvetsa amace cisoni.