Proverbs 10:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa pa munthu wabwino ndi kasupe wa moyo, koma pakamwa pa munthu woipa pamabisa zandeu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kamwa mwa wolungama ndi kasupe wa moyo; koma m'kamwa mwa oipa mubisa chiwawa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakamwa pa munthu wolungama ndi kasupe wamoyo, koma pakamwa pa munthu woyipa pamabisa chiwawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kamwa mwa wolungama ndi kasupe wa moyo; Koma m'kamwa mwa oipa mubisa ciwawa.