Proverbs 10:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chuma cha munthu wolemera ndiye chitetezo chake, koma umphaŵi wa anthu osauka ndiye chiwonongeko chao.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chuma cha wolemera ndi mudzi wake wolimba; koma umphawi wao uononga osauka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chuma cha munthu wolemera ndiye chitetezo chake; koma umphawi ndiye chiwonongeko cha osauka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cuma ca wolemera ndi mudzi wace wolimba; Koma umphawi wao uononga osauka.