Proverbs 10:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Moyo ndiye malipiro a anthu ochita zabwino, koma phindu la ochimwa limadzetsa machimo ena.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ntchito za wolungama zipatsa moyo; koma phindu la oipa lichimwitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Moyo ndiye malipiro a munthu wolungama, koma phindu la anthu oyipa ndi uchimo ndi imfa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nchito za wolungama zipatsa moyo; Koma phindu la oipa licimwitsa.