Proverbs 10:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a munthu wochita zabwino, ali ngati siliva wabwino kwambiri, koma maganizo a anthu oipa ngachabe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Lilime la wolungama likunga siliva wosankhika; koma mtima wa oipa uli wachabe.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mawu a munthu wolungama ali ngati siliva wabwino kwambiri, koma mtima wa munthu woyipa ndi wopanda phindu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Lilime la wolungama likunga siliva wosankhika; Koma mtima wa oipa uli wacabe.