Proverbs 10:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mau a anthu wabwino amaphunzitsa ambiri, koma zitsiru zimafa chifukwa chosoŵa nzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Milomo ya wolungama imadyetsa ambiri; koma zitsiru zimafa posowa nzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Milomo ya anthu olungama imalimbikitsa ambiri; koma chitsiru chimafa chifukwa chosowa nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Milomo ya wolungama imadyetsa ambiri; Koma zitsiru zimafa posowa nzeru.