Proverbs 10:25 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Namondwe akaomba, oipa amachotsedwa, koma anthu ochita chilungamo amakhazikika mpaka muyaya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga kavumbulu angopita, momwemo woipa kuli zii; koma olungama ndiwo maziko osatha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pamene namondwe wawomba, anthu oyipa amachotsedwa, koma anthu olungama amakhazikika mpaka muyaya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga kabvumvulu angopita, momwemo woipa kuti zi; Koma olungama ndiwo maziko osatha.