Proverbs 10:27 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kuwopa Chauta kumatalikitsa moyo, koma zaka za anthu oipa zidzachepa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kuopa Yehova kutanimphitsa masiku; koma zaka za oipa zidzafinimpha.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kuopa Yehova kumatalikitsa moyo; koma zaka za anthu oyipa zidzafupikitsidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kuopa Yehova kutanimphitsa masiku; Koma zaka za oipa zidzafinimpha,