Proverbs 10:29 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta ndi linga loteteza munthu woyenda molungama, koma amaononga wochita zoipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira ya Yehova ndi linga kwa woongoka mtima; koma akuchita zoipa adzaonongeka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Njira za Yehova ndi linga loteteza anthu ochita zabwino, koma wochita zoyipa adzawonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira ya Yehova ndi linga kwa woongoka mtima; Koma akucita zoipa adzaonongeka.