Proverbs 10:3 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta salola kuti munthu womukondweretsa iye, azikhala ndi njala, koma zimene woipa amazilakalaka, Mulungu amam'mana.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova samvetsa njala moyo wa wolungama; koma amainga chifuniro cha wochimwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova salola kuti munthu wolungama azikhala ndi njala; koma amalepheretsa zokhumba za anthu oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova samvetsa njala moyo wa wolungama; Koma amainga cifuniro ca wocimwa.