Proverbs 10:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa pa wochita chilungamo pamatuluka zanzeru, koma lilime lokhota adzalidula.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kamwa mwa wolungama mulankhula nzeru; koma lilime lokhota lidzadulidwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakamwa pa munthu wolungama pamatulutsa za nzeru, koma lilime lokhota lidzadulidwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kamwa mwa wolungama mulankhula nzeru; Koma lilime lokhota lidzadulidwa.