Proverbs 10:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Manja aulesi amagwetsa munthu mu umphaŵi, koma manja achangu amalemeretsa munthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wochita ndi dzanja laulesi amasauka; koma dzanja la akhama lilemeretsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wochita zinthu mwaulesi amasauka, koma wogwira ntchito mwakhama amalemera.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wocita ndi dzanja laulesi amasauka; Koma dzanja la akhama lilemeretsa.