Proverbs 10:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mwana womakolola nthaŵi yachilimwe ndiye wanzeru, koma womangogona nthaŵi yokolola amachititsa manyazi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokolola m'malimwe ndi mwana wanzeru; koma wogona pakutula ndi mwana wochititsa manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene amakolola nthawi yachilimwe ndi mwana wanzeru, koma amene amangogona nthawi yokolola ndi mwana wochititsa manyazi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokolola m'malimwe ndi mwana wanzeru; Koma wogona pakututa ndi mwana wocititsa manyazi.