Proverbs 10:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Madalitso amakhala pa munthu wokondweretsa Mulungu, koma pakamwa pa munthu woipa pamabisa zandeu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Madalitso ali pamtu pa wolungama; koma m'kamwa mwa oipa mubisa chiwawa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Madalitso amakhala pa mutu wa munthu wolungama, koma pakamwa pa munthu woyipa pamaphimba chiwawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Madalitso ali pamtu pa wolungama Koma m'kamwa mwa oipa mubisa ciwawa.