Proverbs 10:7 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wabwino anzake adzamkumbukira ngati dalitso, pamene woipa, mbiri yake idzatha ngati chinthu choola.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amayesa wolungama wodala pomkumbukira; koma dzina la oipa lidzavunda.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wolungama anzake adzamukumbukira ngati mdalitso, koma dzina la munthu woyipa lidzayiwalika.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amayesa wolungama wodala pamkumbukira; Koma dzina la oipa lidzabvunda.