Proverbs 10:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wa mtima wanzeru adzasamala malamulo, koma chitsiru chomangolongolola chidzaonongeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwini mtima wanzeru amalandira malamulo; koma chitsiru cholongolola chidzagwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wa mtima wanzeru amasamala malamulo, koma chitsiru chomangolongolola chidzawonongeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwini mtima wanzeru amalandira malamulo; Koma citsiru colongolola cidzagwa.