Proverbs 11:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wosukitsa anzake ngwopanda nzeru, koma womvetsa zinthu amalonda pakamwa pake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wopeputsa mnzake asowa nzeru; koma wozindikira amatonthola.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wonyoza mnzake ndi wopanda nzeru, koma munthu wanzeru zomvetsa zinthu amakhala chete.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wopeputsa mnzace asowa nzeru; Koma wozindikira amatonthola.