Proverbs 11:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Amene amanka nachita ukazitape, amaulula zinsinsi. Koma wa mtima wokhulupirika, amasunga pakamwa pake.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kazitape woyendayenda amawanditsa zinsinsi; koma wokhulupirika mtima abisa mau.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Amene amanka nachita ukazitape amawulula zinsinsi; koma munthu wokhulupirika amasunga pakamwa pake.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kazitape woyendayenda amawanditsa zinsinsi; Koma wokhulupirika mtima abisa mau.