Proverbs 11:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mkazi wa mkhalidwe wabwino amalandira ulemu, koma amuna ankhanza amangopata chuma.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkazi wodekha agwiritsa ulemu; aukali nagwiritsa chuma.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mkazi wodekha amalandira ulemu, koma amuna ankhanza amangopata chuma.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkazi wodekha agwiritsa ulemu; Aukali nagwiritsa cuma.