Proverbs 11:17 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wachifundo amadzipindulira zabwino, koma munthu wankhwidzi amadzipweteka yekha.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wachifundo achitira moyo wake zokoma; koma wankhanza avuta nyama yake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wachifundo amadzipindulira zabwino koma munthu wankhanza amadzibweretsera mavuto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wacifundo acitira moyo wace zokoma; Koma wankhanza abvuta nyama yace.