Proverbs 11:2 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kunyada kukaloŵa, pamafikanso manyazi, koma pali kudzichepetsa, palinso nzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakudza kudzikuza padzanso manyazi; koma nzeru ili ndi odzichepetsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kunyada kukalowa, pamafikanso manyazi, koma pamene pali kudzichepetsa pameneponso pali nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakudza kudzikuza padzanso manyazi; Koma nzeru iri ndi odzicepetsa,