Proverbs 11:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a mtima woipa amamnyansa Chauta, koma anthu a makhalidwe abwino amamkondweretsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Okhota mtima anyansa Yehova; koma angwiro m'njira zao amsekeretsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova amanyansidwa ndi anthu a mtima wokhotakhota koma amakondwera ndi anthu a makhalidwe angwiro.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Okhota mtima anyansa Yehova; Koma angwiro m'njira zao amsekeretsa.