Proverbs 11:26 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu amatemberera munthu womana anzake chakudya, koma amalemekeza munthu wogulitsa chakudyacho.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Womana tirigu anthu amtemberera; koma madalitso adzakhala pamtu pa wogulitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu amatemberera womana anzake chakudya, koma madalitso amakhala pamutu pa munthu amene amagulitsa chakudyacho.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Womana tirigu anthu amtemberera; Koma madalitso adzakhala pamtu pa wogulitsa.