Proverbs 11:28 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wokhulupirira chuma chake adzafota, koma anthu a Mulungu adzaphukira ngati tsamba laliŵisi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokhulupirira chuma chake adzagwa; koma olungama adzaphuka ngati tsamba.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Aliyense amene amadalira chuma chake adzafota, koma wolungama adzaphukira ngati tsamba lobiriwira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokhulupmra cuma cace adzagwa; Koma olungama adzaphuka ngati tsamba.