Proverbs 11:30 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kukhala moyo wangwiro kumapezetsa moyo, koma kusatsata malamulo kumaononga moyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chipatso cha wolungama ndi mtengo wa moyo; ndipo wokola mtima ali wanzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chipatso cha ntchito zabwino ndi moyo, ndipo kusatsata malamulo kumawonongetsa moyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cipatso ca wolungama ndi mtengo wa moyo; Ndipo wokola mtima ali wanzeru.