Proverbs 11:31 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu abwino amalandira mphotho pa dziko lapansi, koma wochimwa ndi woipa mtima amalandira chilango.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, wolungama adzalandira mphotho kunja kuno; koposa kotani woipa ndi wochimwa?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ngati anthu olungama amalandira mphotho zawo pa dziko lapansi, kuli bwanji anthu osapembedza ndi ochimwa!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, wolungama adzalandira mphotho kunja kuno; Koposa kotani woipa ndi wocimwa?