Proverbs 11:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kulungama kwa anthu angwiro kumaŵathandiza pa moyo wao, koma kuipa mtima kumagwetsa mwiniwake yemweyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chilungamo cha wangwiro chimaongola njira yake; koma woipa adzagwa ndi zoipa zake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chilungamo cha anthu angwiro chimawongolera moyo wawo, koma ntchito zoyipa zimagwetsa mwini wake yemweyo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cilungamo ca wangwiro cimaongola njira yace; Koma woipa adzagwa ndi zoipa zace.