Proverbs 11:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a Mulungu amapulumuka ku mavuto, koma m'malo mwake amagwamo ndi oipa mtima.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wolungama apulumuka kuvuto; woipa nalowa m'malo mwake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wolungama amapulumutsidwa ku mavuto, koma mʼmalo mwake amagwa mʼmavutomo ndi anthu oyipa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolungama apulumuka kubvuto; Woipa nalowa m'malo mwace.