Proverbs 11:9 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wosalabadirako za Mulungu amaononga mnzake ndi pakamwa pake; munthu wochita chilungamo amapulumuka chifukwa cha kudziŵa zinthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wonyoza Mulungu aononga mnzake ndi m'kamwa mwake; koma olungama adzapulumuka pakudziwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wosapembedza amawononga mnansi wake ndi pakamwa pake, koma munthu wolungama amapulumuka chifukwa cha kudziwa zinthu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wonyoza Mulungu aononga mnzace ndi m'kamwa mwace; Koma olungama adzapulumuka pakudziwa,