Proverbs 12:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wokonda mwambo amakonda kudziŵa zinthu, koma wodana ndi chidzudzulo ngwopusa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wokonda mwambo akonda kudziwa; koma wakuda chidzudzulo apulukira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amene amakonda mwambo amakonda kudziwa zinthu, koma amene amadana ndi chidzudzulo ndi wopusa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wokonda mwambo akonda kudziwa; Koma wakuda cidzudzulo apulukira.