Proverbs 12:10 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu wolungama amasamalira moyo wa ziŵeto zake, koma munthu woipa mtima chifundo chake nchankhwidzi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Wolungama asamalira moyo wa choweta chake; koma chifundo cha oipa ndi nkhanza.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu wolungama amasamalira moyo wa ziweto zake, koma chifundo cha munthu woyipa ndi chakhanza.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Wolungama asamalira moyo wa coweta cace; Koma cifundo ca oipa ndi nkhanza.