Proverbs 12:11 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wolima munda wake mwakhama amapeza chakudya chambiri, koma wotsata zopanda pake ngwopanda nzeru.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Zakudya zikwanira wolima minda yake; koma wotsata anthu opanda pake asowa nzeru.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wolima mʼmunda mwake mwakhama adzakhala ndi chakudya chochuluka, koma wotsata zopanda pake alibe nzeru.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Zakudyazikwanira wolima minda yace; Koma wotsata anthu opanda pace asowa nzeru.