Proverbs 12:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu woipa amakodwa mu msampha wa zoipa za pakamwa pake, koma munthu wochita zabwino amapulumuka ku zoipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
M'kulakwa kwa milomo muli msampha woipa; koma wolungama amatuluka m'mavuto.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa; koma munthu wolungama amatuluka mʼmavuto.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
M'kulakwa kwa milomo muli msampha woipa; Koma wolungama amaturuka m'mabvuto.