Proverbs 12:14 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Munthu amalandira zabwino zambiri chifukwa cha mau ake abwino, ntchito zimene munthu amazichita ndi manja ake zimampindulira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Munthu amakhuta zabwino ndi zipatso za m'kamwa mwake; zochita za manja ake zidzabwezedwa kwa iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Munthu amakhala ndi zabwino zambiri chifukwa cha mawu ake ndipo ntchito zimene munthu agwira ndi manja ake zimamupindulira.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Munthu amakhuta zabwino ndi zipatso za m'kamwa mwace; Zocita za manja ace zidzabwezedwa kwa iye.