Proverbs 12:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Zimene amachita munthu wopusa mwiniwakeyo amaziyesa zolungama, koma munthu wanzeru amamvetsera malangizo a ena.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Njira ya chitsiru njolungama pamaso pakepake; koma wanzeru amamvera uphungu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zochita za chitsiru mwini wakeyo amaziona ngati zabwino, koma munthu wanzeru amamvera malangizo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Njira ya citsiru nlolungama pamaso pace pace; Koma wanzeru amamvera uphungu.