Proverbs 12:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kukwiya kwa munthu wopusa kumadziŵika msanga, koma munthu wanzeru salabadako za chipongwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mkwiyo wa chitsiru udziwika posachedwa; koma wanzeru amabisa manyazi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mkwiyo wa chitsiru umadziwika nthawi yomweyo, koma munthu wanzeru sasamala kunyozedwa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mkwiyo wa citsiru udziwika posacedwa; Koma wanzeru amabisa manyazi.