Proverbs 12:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Mumtima mwa anthu opangana zoipa mumakhala kunama, koma anthu olinga zabwino amakhala ndi chimwemwe.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chinyengo chili m'mitima ya oganizira zoipa; koma aphungu a mtendere amakondwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Mʼmitima ya anthu amene amakonza zoyipa muli chinyengo; koma anthu olimbikitsa za mtendere amakhala ndi chimwemwe.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cinyengo ciri m'mitima ya oganizira zoipa; Koma aphungu a mtendere amakondwa.