Proverbs 12:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pakamwa pabodza pamamnyansa Chauta. Koma anthu ochita zinthu mokhulupirika amamkondweretsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Milomo yonama inyansa Yehova; koma ochita ntheradi amsekeretsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakamwa pa bodza pamamunyansa Yehova, koma amakondwera ndi anthu oyankhula zoona.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Milomo yonama inyansa Yehova; Koma ocita ntheradi amsekeretsa.